Baibulo la ana alipo kuti ana amudziwe Yesu Khristu kupyolera muku gawa nthano zambaibulo zojambulidwa, ndi zina zotero mosiyana siyana, kuphatikizapo Wide Web, lamya yammanja/PDA's, zolembedwa pama pepala akalala, mabuku akalala, muchiyankhulidwe chomwe mwana angayankhule.
Mabaibulo awa ndiwo gawila ana 1.8 bilioni apaziko lonse mwaulele momwe zingathekele.